Yoswa 4:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

munene nao, Cifukwa madzi a Yordano anadulidwa patsogolo pa likasa la cipangano ca Yehova; muja lidaoloka Yordano, madzi a Yordano anadulidwa; ndipo miyala iyi idzakhala cikumbutso ca ana a Israyeli cikhalire.

Yoswa 4

Yoswa 4:1-15