Yoswa 19:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo maere aciwiri anamturukira Simeoni, pfuko la ana a Simeoni monga mwa mabanja ao; ndi colowa cao cinali pakati pa colowa ca ana a Yuda.

2. Ndipo anali naco colowa cao Beeri-seba, kapena Seba, ndi Molada;

3. ndi Hazarasuala, ndi Bala, ndi Ezemu;

4. ndi Elitoladi, ndi Betuli, ndi Horimu;

Yoswa 19