Yoswa 13:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pfuko la Levi sanalipatsa colowa; nsembe za Yehova Mulungu wa Israyeli, zocitika ndi moto, ndizo colowa cace, monga iye adanena naye.

Yoswa 13

Yoswa 13:8-22