Yoswa 12:22-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. mfumu ya ku Kadesi, imodzi; mfumu ya ku Yokineamu ku Karimeli, imodzi;

23. mfumuya ku Doro, mpaka ponyamuka pa Doro, imodzi; mfumu ya ku Goimu m'Giligala, imodzi;

24. mfumu ya ku Tiriza, imodzi. Mafumu awa onse ndiwo makumi atatu ndi imodzi.

Yoswa 12