Yohane 9:33-36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

33. Ngatiuyu sanacokera kwa Mulungu, sakadakhoza kucita kanthu.

34. Anayankha natikwa iye, Wabadwa iwe konse m'zoipa, ndipo iwe utiphunzitse ife kodi? Ndipo anamtaya kunja.

35. Yesu anamva kuti adamtaya kunja; ndipo pakumpeza iye, anati, Kodi ukhulupirira Mwana wa Mulungu?

36. Iyeyu anayankha nati, Ndipo ndani iye, Ambuye, kuti ndimkhulupirire iye?

Yohane 9