Yobu 8:19-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. Taona, ici ndico comkondweretsa panjira pace,Ndi panthaka padzamera ena.

20. Taona, Mulungu sakana munthu wangwiro;Kapena kugwiriziza ocita zoipa.

21. Koma adzadzaza m'kamwa mwako ndi kuseka,Ndi milomo yako kupfuula.

Yobu 8