1. Pamenepo anayankha Bilidadi Msuki, nati,
2. Udzanena izi kufikira liti?Ndipo mau a pakamwa pako adzakhala ngati namondwe kufikira liti?
3. Ngati Mulungu akhotetsa ciweruzo?Ngati Wamphamvuyonse akhotetsa mlandu?
4. Cinkana ana ako anamcimwira Iye,Ndipo anawapereka mwa kulakwa kwao;