1. Itana tsono; pali wina wakukuyankha kodi?Ndipo udzatembenukira kwa yani wa oyera mtimawo?
2. Pakuti mkwiyo umapha wopusa,Ndi nsanje imakantha wopanda pace.
3. Ndinapenya wopusa woyala mizu;Koma pomwepo ndinatemberera pokhala pace.
4. Ana ace akhala otekeseka, Napsinjika kucipata,Wopanda wina wakuwapulumutsa.