Yobu 42:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Namuka Elifazi wa ku Temani, ndi Bilidadi Msuki, ndi Zofara wa ku Naama, nacita monga Yehova adawauza; ndipo Yehova anabvomereza Yobu.

Yobu 42

Yobu 42:7-17