Yobu 41:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Kodi opangana malonda adzaitsatsa?Adzaigawana eni malonda?

7. Kodi udzadzaza khungu lace ndi nchetho,Kapena mutu wace ndi miomba?

8. Isanjike dzanja lako;Ukakumbukila nkhondoyi, sudzateronso.

9. Taona, ciyembekezo cako ca pa iyo cipita pacabe.Kodi sadzatenga nkhawa munthu pakungoiona?

Yobu 41