6. Kodi opangana malonda adzaitsatsa?Adzaigawana eni malonda?
7. Kodi udzadzaza khungu lace ndi nchetho,Kapena mutu wace ndi miomba?
8. Isanjike dzanja lako;Ukakumbukila nkhondoyi, sudzateronso.
9. Taona, ciyembekezo cako ca pa iyo cipita pacabe.Kodi sadzatenga nkhawa munthu pakungoiona?