Yobu 38:33-36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

33. Kodi udziwa malemba a kuthambo?Ukhoza kukhazikitsa ufumu wao pa dziko lapansi?

34. Kodi udziwa kukwezera mau ako kumitambo,Kuti madzi ocuruka akukute?

35. Kodi ukhoza kutumiza mphezi kuti zimuke,Ndi kunena nawe, Tiri pano?

36. Ndani analonga nzeru m'mitambomo?Ndani waninkha nyenyezi yotsotsoka luntha?

Yobu 38