12. Koma akapanda kumvera adzatayika ndi lupanga,Nadzatsirizika osadziwa kanthu.
13. Koma iwo a mtima wakunyoza Mulungu, akundika mkwiyo,Akawamanga Iye, sapfuulira.
14. Iwowa akufa akali biriwiri,Ndi moyo wao utayika ngati odetsedwa.
15. Apulumutsa wozunzika mwa kuzunzika kwace,Nawatsegulira m'khutu mwao mwa kupsinjika kwao.