14. Pakuti Mulungu alankhula kamodzi,Kapena kawiri, koma anthu sasamalira.
15. M'kulota, m'masomphenya a usiku,Pakuwagwera anthu tulo tatikuru,Pogona mwacheru pakama,
16. Pamenepo atsegula makutu a anthu,Nakomera cizindikilo cilangizo cao;
17. Kuti acotse munthu ku cimene akadacita,Ndi kubisira munthu kudzikuza kwace;