Yobu 32:17-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Ndidzayankha inenso mau anga,Ndidzaonetsa inenso za m'mtima mwanga.

18. Pakuti ndadzazidwa ndi mau,Ndi mzimu wa m'kati mwanga undifulumiza.

19. Taonani, m'cifuwa mwanga muli ngati vinyo wosowa popungulira,Ngati matumba atsopano akuti aphulike.

20. Ndidzanena kuti cifundo citsike;Ndidzatsegula milomo yanga ndi kuyankha.

Yobu 32