Yobu 31:24-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

24. Ngati ndayesa golidi ciyembekezo canga,Ndi kunena ndi golidi woyengetsa,Ndiwe cikhazikitso canga;

25. Ngati ndinakondwera popeza cuma canga ncacikuru,Ndi dzanja langa lapeza zocuruka;

26. Ngati ndalambira dzuwa lirikuwala,Kapena mwezi ulikuyenda monyezimira;

Yobu 31