24. Ngati ndayesa golidi ciyembekezo canga,Ndi kunena ndi golidi woyengetsa,Ndiwe cikhazikitso canga;
25. Ngati ndinakondwera popeza cuma canga ncacikuru,Ndi dzanja langa lapeza zocuruka;
26. Ngati ndalambira dzuwa lirikuwala,Kapena mwezi ulikuyenda monyezimira;