Yobu 30:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Koma tsopano iwo osafikana msinkhu wanga andiseka,Iwo amene atate ao ndikadawapeputsa, osawaika pamodzi ndi agaru olinda nkhosa zanga.

2. Mphamvunso ya m'manja mwao ndikadapindulanji nayo?Ndiwo anthu amene unyamata wao udatha,

Yobu 30