24. Pakuti ndikati ndidye, kumadza kuusa moyo kwanga;Ndi kudzuma kwanga kumathiridwa ngati madzi.
25. Pakuti cimene ndinaciopa candigwera,Ndi cimene ndacita naco mantha candidzera.
26. Wosakhazikika, ndi wosakhala cete, ndi wosapumula ine,Koma mabvuto anandidzera.