14. Pamodzi ndi mafumu ndi maphungu a padziko,Akudzimangira m'mabwinja;
15. Kapena pamodzi ndi akalonga eni ace a golidi,Odzaza nyumba zao ndi siliva;
16. Kapena ngati nsenye yobisika ndikadakhala kuli zi;Ngati makanda osaona kuunika.
17. Apo oipa aleka kumabvuta;Ndi apo ofoka mphamvu akhala m'kupumula.