Yobu 29:23-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

23. Anandilindira ngati kulindira mvula,Nayasama pakamwa pao ngati kulira mvula ya masika.

24. Ndinawaseka akapanda kulimbika mtima;Ndipo sanagwetsa kusangalala kwa nkhope yanga.

Yobu 29