Yobu 29:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Yobu anaonjezanso mwambi wace, nati,

2. Ha! ndikadakhala monga m'miyezi yapitayi,Monga m'masiku akundisunga Mulungu;

3. Muja nyali yace inawala pamutu panga,Ndipo ndi kuunika kwace ndinayenda mumdima;

4. Monga umo ndinakhala m'masiku anga olimba,Muja uphungu wa Mulungu unakhala pahema panga;

Yobu 29