8. Pakuti aponyedwa m'ukonde ndi mapazi ace,Namaponda pamatanda.
9. Msampha udzamgwira kucitende,Ndi khwekhwe lidzamkola.
10. Msampha woponda umbisikira pansi,Ndi msampha wa cipeto panjira.
11. Zoopetsa zidzamcititsa mantha monsemo,Nadzampitikitsa kumbuyo kwace.