12. Zisanduliza usiku ukhale usana;Kuunika kuyandikana ndi mdima.
13. Ndikayembekezera kumanda kukhale nyumba yanga;Ndikayala pogona panga mumdima.
14. Ndikati kwa dzenje, Ndiwe atate wanga;Kwa mphutsi, Ndiwe mai wanga ndi mlongo wanga;
15. Ciri kuti ciyembekezo canga?Inde, ciyembekezo canga adzaciona ndani?