Yobu 13:26-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

26. Pakuti mundilembera zinthu zowawa,Ndi kundipatsa ngati colowa mphulupulu za ubwana wanga.

27. Mulonganso mapazi anga m'zigologolo, ndi kupenyerera mayendedwe anga onse;Mudzilembera malire mopanika mapazi anga;

28. Momwemo munthu akutha ngati cinthu coola,Ngati cobvala codyedwa ndi numbi

Yobu 13