Yobu 10:20-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

20. Masiku anga satsala owerengeka nanga? lindani,Bandilekani kuti nditsitsimuke pang'ono,

21. Ndisanacoke kumka kumene sindikabweranso,Ku dziko la mdima ndi la mthunzi wa imfa;

22. Dziko la mdima bii ngati mdima wandiweyani,Dziko la mthunzi wa imfa losalongosoka,Kumene kuunika kukunga mdima.

Yobu 10