20. Masiku anga satsala owerengeka nanga? lindani,Bandilekani kuti nditsitsimuke pang'ono,
21. Ndisanacoke kumka kumene sindikabweranso,Ku dziko la mdima ndi la mthunzi wa imfa;
22. Dziko la mdima bii ngati mdima wandiweyani,Dziko la mthunzi wa imfa losalongosoka,Kumene kuunika kukunga mdima.