Yobu 1:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo taonani, inadza mphepo yaikuru yocokera kucipululu, niomba pa ngondya zonse zinai za nyumbayo, nigwa pa anyamatawo, nafa; ndipo ndapulumuka ine ndekha kudzakuuzani.

Yobu 1

Yobu 1:16-20