Yesaya 8:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Iye adzakhala malo opatulika; koma mwala wopunthwitsa, ndi thanthwe lolakwitsa la nyumba zonse ziwiri za Israyeli, khwekhwe ndi msampha wa okhala m'Yerusalemu.

Yesaya 8

Yesaya 8:4-15