Yesaya 66:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti atero Yehova, Taonani ndidzamfikitsira mtendere ngati mtsinje, ndi ulemerero wa amitundu ngati mtsinje wosefukira. Inu mudzayamwa, ndi kunyamulidwa pambali, ndi kululuzidwa pa maondo,

Yesaya 66

Yesaya 66:11-21