Yesaya 60:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tukula maso ako uunguze-unguze ndi kuona; iwo onse asonkhana pamodzi, adza kwa iwe; ana ako amuna adzacokera kutari, ndi ana ako akazi adzaleredwa pambali.

Yesaya 60

Yesaya 60:1-6