Yesaya 57:20-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

20. Koma oipa ali ofanana ndi nyanja yowinduka; pakuti siingapume, ndi madzi ace autsa matope ndi ubve.

21. Palibe mtendere, ati Mulungu wanga, kwa oipa.

Yesaya 57