Yesaya 55:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

M'malo mwa mithethe mudzaturuka mtengo wamlombwa; ndi m'malo mwa lunguzi mudzamera mtengo wamcisu; ndipo cidzakhala kwa Yehova ngati mbiri, ngati cizindikiro cosatha, cimene sicidzalikhidwa.

Yesaya 55

Yesaya 55:9-13