Yesaya 54:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti Mlengi wako ndiye mwamuna wako; Yehova wa makamu ndiye dzina lace; ndi Woyera wa Israyeli ndiye Mombolo wako; Iye adzachedwa Mulungu wa dziko lonse lapansi.

Yesaya 54

Yesaya 54:1-9