Yesaya 52:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace kodi ndicitenji pano? ati Yehova; popeza anthu anga acotsedwa popanda kanthu? akuwalamulira awaliritsa, ati Yehova; ndipo dzina langa licitidwa mwano tsiku lonse kosalekeza.

Yesaya 52

Yesaya 52:2-14