Yesaya 50:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti Ambuye Yehova adzandithangata Ine; cifukwa cace sindinasokonezedwa; cifukwa cace ndakhazika nkhope yanga ngati mwala, ndipo ndidziwa kuti sindidzakhala ndi manyazi.

Yesaya 50

Yesaya 50:1-9