Yesaya 47:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Taima tsopano ndi maphendo ako, ndi unyinji wa matsenga ako, m'menemo iwe unagwira nchito ciyambire ubwana wako; kuti kapena udzatha kupindula, kuti kapena udzapambana.

Yesaya 47

Yesaya 47:7-15