Yesaya 45:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsoka kwa iye amene akangana ndi Mlengi wace! phale mwa mapale a dziko lapansi! Kodi dongo linganene kwa iye amene aliumba, Kodi upanga ciani? pena nchito yako, Iye alibe manja?

Yesaya 45

Yesaya 45:2-11