Yesaya 44:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Omwe apanga fano losema onsewo asokonezeka; ndipo zokondweretsa zao sadzapindula nazo kanthu; ndipo mboni zao siziona, kapena kudziwa; kuti akhale ndi manyazi.

Yesaya 44

Yesaya 44:5-19