Yesaya 43:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Amitundu onse asonkhane pamodzi, ndi anthu aunjikane; ndani mwa iwo anganene ici ndi kuonetsa ife zinthu zakale? atenge mboni zao, kuti abvomerezeke ndi olungama; pena amve, nanene zoonadi.

Yesaya 43

Yesaya 43:1-11