Yesaya 43:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pokhala iwe wa mtengo wapatari pamaso panga, ndi wolemekezeka, ndipo ndakukonda iwe; Ine ndidzakuombola ndi anthu, ndi kupereka anthu m'malo mwa moyo wako.

Yesaya 43

Yesaya 43:1-6