Yesaya 42:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace anatsanulira pa iye mkwiyo wace waukali, ndi mphamvu za nkhondo; ndipo unamyatsira moto kuzungulira kwace, koma iye sanadziwa; ndipo unamtentha, koma iye sanacisunga m'mtima.

Yesaya 42

Yesaya 42:23-25