Yesaya 40:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mau a wina ati, Pfuula. Ndipo ndinati, Kodi ndipfuule ciani? Anthu onse ndi udzu, ndi kukoma kwao konse kunga duwa la m'thengo;

Yesaya 40

Yesaya 40:1-9