Yesaya 38:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

taona, ndidzabweza mthunzi wa pamakwerero, umene watsika pa makwerero a Ahazi ndi dzuwa, ubwerere makwerero khumi. Ndipo dzuwa linabwerera makwerero khumi pamakwerero, pamene udatsika mthunziwo.

Yesaya 38

Yesaya 38:5-14