Yesaya 38:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ambuye ndi zinthu izi anthu akhala ndi moyo.Ndipo m'menemo monse muli moyo wa mzimu wanga;Cifukwa cace mundiciritse ine,Ndi kundikhalitsa ndi moyo.

Yesaya 38

Yesaya 38:7-22