Yesaya 35:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mcenga wong'azimira udzasanduka thamanda, ndi nthaka yopanda madzi idzasanduka zitsime zamadzi; m'malo a ankhandwe m'mene iwo anagona, mudzakhala udzu ndi mabango ndi milulu.

Yesaya 35

Yesaya 35:1-10