Yesaya 33:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Zingwe zako za ngalawa zamasulidwa; sizinathe kulimbitsa patsinde pa mlongoti wace, sizinathe kufutukula matanga; pamenepo ndipo colanda cacikulu, cofunkha cinagawanidwa; wopunduka nafumfula.

Yesaya 33

Yesaya 33:18-24