Yesaya 25:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa Inu mwakhala linga la aumphawi, linga la osowa m'kubvutidwa kwace, pobisalira cimphepo, mthunzi wa pa dzuwa, pamene kuomba kwa akuopsya kufanana ndi cimphepo cakuomba chemba.

Yesaya 25

Yesaya 25:1-12