Yesaya 25:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa m'phiri limeneli dzanja la Yehova lidzakhalamo, ndipo Moabu adzaponderezedwa pansi m'malo ace, monga maudzu aponderezedwa padzala.

Yesaya 25

Yesaya 25:6-12