Yesaya 2:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa inu mwasiya anthu anu a nyumba ya Yakobo, cifukwa kuti iwo adzazidwa ndi miyambo ya kum'mawa, ndipo ali olaula ngati Afilisti, naomba m'manja ndi ana a acilendo.

Yesaya 2

Yesaya 2:5-14