Yesaya 19:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova wasanganiza mzimu wa kusaweruzika pakati pace; ndipo iwo asoceretsa Aigupto m'nchito zonse zace, monga mwamuna woledzera ayenda punzipunzi posanza pace.

Yesaya 19

Yesaya 19:8-18