Yesaya 11:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo padzakhala tsiku lomwelo, kuti muzu wa Jese umene uima ngati mbendera ya mitundu ya anthu, amitundu adzafunafuna uwu; ndipo popuma pace padzakhala ulemerero.

Yesaya 11

Yesaya 11:9-15