Yesaya 10:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo adzanyeketsa ulemerero wa m'nkhalango yace, ndi wa m'munda wace wopatsa bwino, moyo ndi thupi; ndipo padzakhala monga ngati pokomoka wonyamula mbendera.

Yesaya 10

Yesaya 10:8-27